22/09/2024
Zonse chifukwa chosawa ulamuliro wabwinoðŸ˜ðŸ’”
Oyendetsa galimoto ena komanso achibale a dalaiva yemwe zikumveka kuti waombeledwa ndi apolisi pa road block ya 4 miles ku Zomba ayamba kusonkhana ku polisi ya Zomba.
Titafika pamalopa tapeza achibale a malemuwa akulira pa polisiyi ndipo oyendetsa galimoto ataima pa polisiyi.
Ena mwa omwe anali nawo mgalimotoyi padakali pano akuwalemba ma statement.
Wolemba Tiyese Monjeza.
Copied (times 360 Malawi)