Malawi wanga

Malawi wanga This is the Entertainment Arm of .Trending updates on malawian celebrities,Entertainment,News and many more
✔️ Follow
✔️Like
✔️Share
(7)

Mu chaka cha 1979 nzimayi ochedwa Elvita Adams ankafuna kuzipha poziponya pansi kuchoka pa nyumba yaitali kwambiri floor...
13/05/2026

Mu chaka cha 1979 nzimayi ochedwa Elvita Adams ankafuna kuzipha poziponya pansi kuchoka pa nyumba yaitali kwambiri floor number 86

Chinachitika nchoti ataziponya mphepo inamukhankhira mbali zosatira zake anakagwera floor ya lchi 85 kuchoka 86 sanakafike pansi. Anavulala fupa lathako kma anapulumuka. Nkhaniyi inqchitika ku New York.

SIDENOTE
Nthawi zina mavuto amazakuchurukira mpkana imfaso kukukana. DO NOT COMMIT SU***DE, it is not a solution and it will never be.

Ndife odalilika tiyeseni lero ndipo simudzakhumudwa❤
13/05/2026

Ndife odalilika tiyeseni lero ndipo simudzakhumudwa❤

 Kambuku (leopard) waonedwa akungozungulira-zungulira pafupi ndi campus ya University of Livingstonia yomwe ili ku Kanin...
13/05/2026


Kambuku (leopard) waonedwa akungozungulira-zungulira pafupi ndi campus ya University of Livingstonia yomwe ili ku Kaning'ina mu Mzinda wa Mzuzu

Samalani mayendedwe anu

Zimai wina ku mzimba watemedwa mutu ndi khasu ndi mkazi zake chifukwa cha Nsanje.Bambo Scochi Jere ku Mzimba adakwatira ...
13/05/2026

Zimai wina ku mzimba watemedwa mutu ndi khasu ndi mkazi zake chifukwa cha Nsanje.

Bambo Scochi Jere ku Mzimba adakwatira akazi awiri, ndipo iwowa anali kukonda kwambiri mkazi wachiwiriyo, ndipo nthawi zambiri adali kukagona kwa mkazi wachiwiriyo, masiku apitawa adaganiza zoti akagone kwa mkazi wawo woyamba, basiti mkazi wachiwiri anatenga khasu mkumutema nalo mutu mkazi oyambayo

Video in comment section

🚨🚨🚨🚨🚨🚨EMERGENCY 🫵🫵🫵🫵🫵🫵South Africa 🇿🇦 si nkhalango ya cr!me kapena hatr€d, ndipo sitidzalola kuona gulu la anthu likumen...
13/05/2026

🚨🚨🚨🚨🚨🚨
EMERGENCY 🫵🫵🫵🫵🫵🫵

South Africa 🇿🇦 si nkhalango ya cr!me kapena hatr€d, ndipo sitidzalola kuona gulu la anthu likumenyana ndi nzika zakunja kapena othawa kwawo.

Boma la South Africa nthawi zonse lakhala likuonetsetsa kuti lili ndi udindo kwa othawa kwawo okhala ku South Africa, ndipo tidzaonetsetsa kuti onse alembedwa.

Sitikukumana ndi mavuto ndi omwe akuchita ziwonetsero zotsutsana ndi boma, koma tili ndi mavuto ndi omwe akuchita ziwonetsero ndikulimbana ndi anthu osalakwa omwe akuyesera kupeza ndalama.

Boma la South Africa sililola nzika iliyonse kupempha anthu zikalata, zilolezo zogwirira ntchito, kapena chitetezo, chifukwa simungathe kusiyanitsa zomwe zili zoyambirira ndi zabodza. NOTE 👊👊👊👊
ine ndilibe thawi yobwelesa khani yofookesa kapena kukhumudwisa kwamuthu yemwe akufuna kapena akukonzeka kubwera kuno ndiudindo wanga pa page pano kukupasirani zofookesa koma nasakha kukupasirani zabwino bansi mukafuna zofookesa pitani ma page mwinamo koma pano simuzakhumudwa ndipo palibepo matha aliwonse✌️✌️✌️

director hendede by TAKULANDIRANI PATHEBA 🇿🇦🇲🇼🇿🇦🇲🇼🇿🇦🇲🇼✌️✌️✌️✌️✌️

Komano mwina zinazi zimakhala ziwanda chabe Nanga nkazi wabwinobwino ngati uyu mpaka kuluma neba nkhutu mpaka kulichotsa...
13/05/2026

Komano mwina zinazi zimakhala ziwanda chabe Nanga nkazi wabwinobwino ngati uyu mpaka kuluma neba nkhutu mpaka kulichotsapo nkhani yake walowa nyumba iye akukolopamo mmmmh 😢

13/05/2026

Koma kineo Wakulakwirani Chani😂

 ! Ngakhale mfumu Rabson yakwa Mfumu yaikulu Kanduku m'boma la Mwanza inakaniza maliro a Gogo Nasimango Mateche, wazaka ...
13/05/2026

!
Ngakhale mfumu Rabson yakwa Mfumu yaikulu Kanduku m'boma la Mwanza inakaniza maliro a Gogo Nasimango Mateche, wazaka 104, kuti ayikidwe m'manda mwake anthu okwiya ammudzi atsekula kumanda ndipo manda ayamba kukumbidwa.

Mmene nthawi imakwana 3:30 masana manda oti Gogoyu ayikidwe mkuti atayamba kukumbidwa.

Koma mfumu Kanduku yafotokoza kuti iyoyo siikudziwa kuti kuli maliro ena alionse agule ndipo iyo siinaletse mfumu yake kuloleza anthu kuika maliro awo.

Poyifunsa mfumu Rabson titayiipeza mmudzimu yati iyo siinganenepo kanthu kalikonse pankhaniyi.

Gilbert Mbewe wammudzi mwa Rabson wati zomwe apanga mafumuwa nzokhumudwitsa kwambiri chifukwa uku nkusankhana mitundu.

Iye wati mafumuwa amayenela kulola angoni ndi achewa kuti adzikhalira limodzi powalolera kukhalira limodzi.

 ANA AWIRI AMWALIRA PA NGOZI YAPA MSEWU M'BOMA LA MANGOCHIAna awiri amwalira pa 11 May 2026 atagundidwa ndi galimoto pom...
12/05/2026


ANA AWIRI AMWALIRA PA NGOZI YAPA MSEWU M'BOMA LA MANGOCHI

Ana awiri amwalira pa 11 May 2026 atagundidwa ndi galimoto pomwe amaoloka msewu m'mudzi wa Sumaili, msewu wa Bakili Muluzi Highway m'boma la Mangochi.

Mneneri wa polisi ya Mangochi Amina Tepani Daudi wati awiriwa ndi a Sharif Duwa a zaka khumi (10) ndi a Kifa Charles a zaka zisanu ndi zinayi (9).

A Daudi ati kafukufuku wawo wapedza kuti a Shafi Kassim azaka 28 omwe amayendetsa galimoto la mtundu wa Toyota Sienta namabala yake MH 111C amachokera mtunda wa Chiponde kulunjika ku Mangochi boma pomwe anachita ngoziyi.

"Ngoziyi yachitika kamba koti galimoto imathamang kwambiri ndipo dalaivalayu anathawa pamalo angoziwa ndikusiya galimoto pomwepo". Atero a Daudi.

Malingana ndi a Daudi, anawa anavulala kwambiri m'mutu ndipo anathamangira nawo pa chipatala cha Namwera komwe achipatala anatsimikiza kuti anali atamwalira kale.

M'mawa wapa 12 May 2026 oganiziridwawa anakadzipereka okha ku polisi ndipo akuyembekezereka kuyankha mlandu opha munthu kamba koyendetsa galimoto mosasamala.

Anawa amachokera m'mudzi mwa Salimu kwa T/A Jalasi m'boma la Mangochi.

"Uniform Ya Asilikali Siyoseweletsa"__Pali mphekesera zoti Model komanso Actress Sophie Mphonda wachotsesa ntchito munth...
12/05/2026

"Uniform Ya Asilikali Siyoseweletsa"

__Pali mphekesera zoti Model komanso Actress Sophie Mphonda wachotsesa ntchito munthu amene anamubwereka yunifolomu ya usilikali iyi kuti agwiritse ntchito pa za umodel pa tsiku la Labour Day.

Malamulo a Malawi amati chani zokhuza Uniform ya Asilikari:

__Only authorized MDF personnel can wear official military uniforms.

__ Civilians are not allowed to wear army camouflage, ranks, badges, or outfits that closely resemble MDF uniforms.

__ Even a member of the MDF can be punished for wearing a uniform they are not authorized to wear.

__Breaking the rule can lead to confiscation, arrest, fines, or imprisonment.
Umatha Daily

Address

Lilongwe

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Malawi wanga posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Organization

Send a message to Malawi wanga:

Share