DPP Diaspora RSA WING

DPP Diaspora RSA WING DPP Diaspora RSA Wing is a branch of dedicated DPP supporters living in South Africa.

Our aim is to unite Malawians in the diaspora to discuss and implement ways to support and contribute to the development of our country MALAWI

DPP RSA:Mu ndale, mpikisano usakhale chifukwa chodana. M’malo mwake, ukhale mwayi wophunzira, kugwirizana ndikutumikira ...
07/08/2026

DPP RSA:

Mu ndale, mpikisano usakhale chifukwa chodana. M’malo mwake, ukhale mwayi wophunzira, kugwirizana ndikutumikira dziko.

Ndizosangalatsa kuona atsogoleri achinyamata akuwonetsa kuti mgwirizano ndi kukhulupirirana zingabweretse zotsatira zabwino. Tikamaona Hon. Leonard Chimbanga, First Secretary ku Malawi High Commission ku Pretoria, ndi Hon. Minister of Youth Sports & Culture-Hon Alfred Gangata,MP akugwira ntchito mwaulemu komanso mogwirizana pa maudindo awo, zimatiphunzitsa kuti ulemu, kulumikizana ndi mgwirizano ndizofunika kwambiri pa utsogoleri.

Achinyamata andale tiyeni tiphunzire kuti kupambana sikumachokera pa kunyozana koma pa kugwira ntchito limodzi, kulemekezana, komanso kuthandizana kuti dziko lipite patsogolo.

Tikakhala ogwirizana, timakhala amphamvu. Tikamakhulupirirana, timatha kukwaniritsa zolinga zazikulu.

Dziko limamangidwa ndi anthu omwe amasankha mgwirizano osati mikangano.

President Arthur Peter Mutharika akugwira ntchito yosula achinyama kuti azakhale atsogoleri a mawa.

Tiyeni achinyamata titengerepo phunziro.

Democratic Progressive Party - DPP

DPP RSA:DPP Diaspora RSA Wing si kungokhala gulu la ndale, koma ndi banja la anthu.Pamene m’bale kapena mlongo wathu aku...
06/08/2026

DPP RSA:

DPP Diaspora RSA Wing si kungokhala gulu la ndale, koma ndi banja la anthu.

Pamene m’bale kapena mlongo wathu akumana ndi mavuto, timakhala limodzi. Pamene pali maliro, timathandizana. Pamene pali nkhani zokhudza ufulu ndi moyo wa a Malawi okhala ku South Africa, timayankhula ndi kuyimira nzika zathu.

Takhulupirira kuti mphamvu ya mgwirizano ndi imene imapanga kusiyana. Cholinga chathu ndi kulimbikitsa umodzi, kuthandizana, komanso kukhala mawu a aMalawi onse omwe ali kunja kwa dziko.

Pamodzi tili amphamvu. Pamodzi timamanga tsogolo labwino.



Democratic Progressive Party - DPP Leonard Chimbanga

05/08/2026

DPP RSA:

President wadziko lathu Professor Peter Mutharika wachona mziko mo ndipo ali mu dziko lino la South Africa paulendo wake omwe akuti ndiwachinsinsi osati waboma.

Mu Video yi ndimomwe anasanzikila muchingerezi.

Democratic Progressive Party - DPP

05/08/2026

DPP RSA:

Mkulukuta moyo kukumbusa abale a UTM kuti anachokela ku kholo lomweli and anasankha kukawinisa anthu ankhanza ndikukafinyidwako😂

Keep resting in peace mwana wa adadi MALU MALU you were always there for DPP, Malawi or South Africa sunawasiye adadi🕊️

Democratic Progressive Party - DPP

DPP RSA:Anthu ambiri ayamikila mgwirizano, umodzi ndi kudzipereka komwe mamembala a DPP Diaspora RSA Wing awonetsa poten...
03/08/2026

DPP RSA:

Anthu ambiri ayamikila mgwirizano, umodzi ndi kudzipereka komwe mamembala a DPP Diaspora RSA Wing awonetsa potenga nawo gawo poonetsetsa kuti maliro a mmodzi wa anzathu, malemu Mr. Lawrence Mphepo ayenda mwaulemu komanso mwadongosolo.

Kuyambira pokonzekera maliro, kuthandizana ndi banja la malemu, kufikira tsiku la maliro, mamembala onse anasonyeza chikondi, ulemu ndi mzimu wa umodzi. Izi zikusonyeza kuti DPP Diaspora RSA Wing si bungwe la ndale lokha koma ndi banja lomwe limayimilira limodzi pa nthawi ya chisomo komanso pa nthawi ya masautso.

Tikuthokoza aliyense amene anapereka nthawi yake, mphamvu zake, chuma chake ndi mapemphero ake kuti zonse ziyende bwino. Mgwirizano umenewu ndi chitsanzo chabwino kwa ena, ndipo ukupitiriza kulimbikitsa ubale ndi chikondi pakati pa a DPP Diaspora RSA Wing.

Pamodzi timakhala amphamvu. Pamodzi timatonthozana. Pamodzi timamanganso chiyembekezo.

Democratic Progressive Party - DPP

03/08/2026

DPP RSA:

Zinthu zikutheka ndithu pano and boma likuyesesa kuti miseu ikhonzedwe maka maka nzeu uwuwu wa Blantyre to Lilongwe wu sunalibwino kwambiri.

Tiyamikile mkulukutamoyo pantchito yabwinoyi.

03/08/2026

DPP RSA:

Yesterday, the DPP Diaspora RSA Wing bid a heartfelt farewell to one of our own, our beloved Advisor Mr. Lawrence Mphepo, who was laid to rest in an emotional ceremony attended by family, friends, comrades and members of the community.

It was a day filled with sorrow, reflection and gratitude as we celebrated the life of a man whose wisdom, guidance and dedication left a lasting impact on the DPP Diaspora family. Though our hearts are heavy, we take comfort in the legacy he leaves behind.

On behalf of the entire DPP Diaspora RSA Wing, our Publicity Secretary delivered a moving tribute, expressing our deepest condolences to the bereaved family and thanking everyone who stood with us during this difficult time. The speech reflected the unity, love and respect that Mr. Mphepo earned throughout his life.

To the Mphepo family, may you find strength and comfort in the love and prayers of those around you. As the DPP Diaspora RSA Wing, we remain united in mourning the loss of our Advisor and committed to preserving the values he stood for.

Rest in eternal peace Mr. Lawrence Mphepo. Your counsel, humility and service will never be forgotten. May your soul continue to rest in God’s eternal glory.

May his memory continue to be a blessing to his family, friends and the entire DPP Diaspora RSA Wing.

GO AND REST OUR COMRADE🕊️

Democratic Progressive Party - DPP Leonard Chimbanga Arthur Peter Mutharika

Today, with heavy hearts, we bid our final farewell to our beloved Advisor Mr. Lawrence Mphepo who will be laid to rest....
02/08/2026

Today, with heavy hearts, we bid our final farewell to our beloved Advisor Mr. Lawrence Mphepo who will be laid to rest.

REST IN PEACE OUR ADVISOR, FATHER AND MENTOR🕊️

Democratic Progressive Party - DPP Leonard Chimbanga

DPP RSA:DPP DIASPORA RSA WING ENGAGES HON. KAMULEPO KALUA ON DIASPORA WELFAREThe DPP Diaspora RSA Wing held a productive...
31/07/2026

DPP RSA:

DPP DIASPORA RSA WING ENGAGES HON. KAMULEPO KALUA ON DIASPORA WELFARE

The DPP Diaspora RSA Wing held a productive engagement with Hon. Kamulepo Kalua in South Africa, where discussions focused on matters affecting Malawians living in the diaspora, with particular attention given to the welfare and repatriation of stranded Malawians.

The meeting reaffirmed the importance of collaboration between the party leadership and the diaspora in finding practical solutions to challenges facing Malawian citizens abroad. Hon. Kalua commended the continued commitment and humanitarian efforts being demonstrated by members of the DPP Diaspora RSA Wing in supporting fellow Malawians during difficult times.

The meeting was attended by DPP Diaspora RSA Wing executive members, including Governor Mr. Mike Nyirenda, Recruitment Director Mrs. Abit Thandi Tefu, Vice Women Director Miss Judith Kalua, and Treasurer Mr. MD Mweso.

As the DPP Diaspora RSA Wing, we remain committed to serving Malawians with dedication, compassion, and unity. We encourage all members to continue working together in the spirit of solidarity, knowing that through unity we can make a meaningful difference in the lives of our fellow citizens.

Democratic Progressive Party - DPP Leonard Chimbanga

🕊️SEND-OFF UPDATE – LATE LAWRENCE MPHEPO 🕊️The DPP Diaspora RSA Wing extends its deepest condolences to the family, rela...
30/07/2026

🕊️SEND-OFF UPDATE – LATE LAWRENCE MPHEPO 🕊️

The DPP Diaspora RSA Wing extends its deepest condolences to the family, relatives, and friends of our departed brother, Lawrence Mphepo.

We wish to inform all Malawians in South Africa, DPP members, and well-wishers that the send-off ceremony for the late Lawrence Mphepo will take place as follows:

📅 Date: Sunday, 2 August 2026
🕗 Time: 8:00 AM

📍 Send-Off Ceremony Venue:
Thabong Conference Centre
172A Witpoortjie Road
Rand Collieries SH
Brakpan 1540

⚰️ Burial Venue:
Van Dyk Cemetery
Barry Marais Road
Leeuwpoort 113-Ir
Boksburg

🍽️ Refreshments:
The venue for refreshments after the burial will be communicated in due course.

We encourage all DPP members, Malawians living in South Africa, and friends of the family who are able to attend to join us in giving our beloved brother a dignified and respectful farewell.

May the Almighty God comfort the bereaved family during this difficult time and grant the late Lawrence Mphepo eternal rest.

Issued by: Vice Director of Events
DPP Diaspora RSA Wing

Address

Pretoria

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when DPP Diaspora RSA WING posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share