Democratic Progressive Party - DPP

Democratic Progressive Party - DPP This is the Official page of the Democratic Progressive Party in Malawi The Democratic Progressive Party (DPP) is a political party in.
(4)

The party was formed in February 2005 by Former President of the Republic of Malawi, His Excellency Ngwazi Professor Bingu Wa Mutharika.

05/09/2026

Mkhunda zonse zauluka chaka chino ku mkumano wa angoni.

Mu 2025 mkhunda ya Chakwera inakana kuwuluka. Zomwe zinaonetsela kuti Chakwera wakanidwa

05/09/2026
God bless the King Arthur Peter Mutharika
05/09/2026

God bless the King Arthur Peter Mutharika

Koma izizi zinali zachani? Kuloncha sitima yoti sikufika ndiku Nsanje komwe. Amfumu Chimombo mmasekerera izizi? Lero zil...
04/09/2026

Koma izizi zinali zachani? Kuloncha sitima yoti sikufika ndiku Nsanje komwe. Amfumu Chimombo mmasekerera izizi? Lero zilipati? Ndalama zinapita kuti?

MINISTER MWANAMVEKHA COMMENDS MRA STAFF AT DEDZA BORDER FOR DILIGENCE AND MEETING REVENUE TARGETSThe Honourable Joseph M...
02/09/2026

MINISTER MWANAMVEKHA COMMENDS MRA STAFF AT DEDZA BORDER FOR DILIGENCE AND MEETING REVENUE TARGETS

The Honourable Joseph Mathyola Mwanamvekha, MP, Minister of Finance and Economic Planning, yesterday commended officers of the Malawi Revenue Authority at the Dedza Border for their professionalism, commitment and for consistently meeting revenue collection targets.

The Minister made the remarks during a working visit to the border post. The purpose of the visit was to appreciate the daily challenges faced by staff and to find practical solutions to improve service delivery.

One of the key challenges raised was the shortage of computers, which slows down operations and puts extra pressure on officers.

Hon. Mwanamvekha assured the team that under the leadership of His Excellency Professor Arthur Peter Mutharika and the Democratic Progressive Party administration, these challenges will be addressed as a matter of priority. He noted that a well-equipped and motivated workforce is central to increasing government revenue and protecting the economy.

Accompanying the Minister were Dr. Cliff Chiunda, Secretary to the Treasury, and senior officials from the Ministry of Finance.

The Minister applauded the MRA staff at Dedza for their patriotism and hard work. He said their contribution is vital to building a stronger Malawi, where public services are funded and development projects are delivered on time.

The DPP administration remains committed to supporting frontline institutions like the MRA with the necessary tools and resources so that officers can serve Malawians with efficiency, integrity and pride.

Dedza - Malawi Mwanamvekha Arrives at Dedza Border Post for Tour of DutyMinister of Finance, Economic Planning and Decen...
02/09/2026

Dedza - Malawi

Mwanamvekha Arrives at Dedza Border Post for Tour of Duty

Minister of Finance, Economic Planning and Decentralization, Hon. Joseph Mathyola Mwanamvekha, MP, has arrived at the Dedza Border Post, where he is expected to conduct a tour of duty at the Malawi Revenue Authority (MRA) offices and assess some of the challenges being faced at the border.

Mwanamvekha is accompanied by Secretary to the Treasury, Dr. Cliff Chiunda, and other senior officials from the Ministry of Finance.

The visit marks Mwanamvekha’s second tour of a border post in recent weeks, following his visit to the Mchinji–Mwami One Stop Border Post last month.

The tour is expected to provide the Minister with an opportunity to appreciate the operations at the border, engage with officials and assess challenges affecting the smooth movement of people and goods.

Wachiwiri kwa Nduna yazachitetezo komanso yemwe ali phungu wa chipani cha DPP ku Ntcheu Central Central East Norman Chis...
29/08/2026

Wachiwiri kwa Nduna yazachitetezo komanso yemwe ali phungu wa chipani cha DPP ku Ntcheu Central Central East Norman Chisale lero wapeleka magalimoto achipatala choyenda (Ambulance) awiri ndi ma Track awiri omwe azitumikira ku Nkhani yaza umoyo komanso chitukuko Cha m'delari.

Poyankhula pa mwambo opeleka zipangizodzi, chi Chisale wati awonesesa kuti umoyo wa anthu okhala mu dela lawo wasintha.

Chisale wapempha anthu okhala mu m'delali kuti asamale zitukuko zomwe alandira komanso zikhale zikubwera mudzimu.

Pamwambowu Norman Chisale wapeleka thumba la ufa, Nsalu komanso ndalama yogulira ndiwo kwa anthu achikulire okwana 600.

29/08/2026

Kuli Chimwemwe kumudzi kwa Senior Chief champiti pomwe Phungu wa nyumba yamalamulo ku Ntcheu Central Central East a Norman Chisale abwera kuzasiya ma Ambulance, ma lorry awiri othandizira mu constituency komanso zakudya kwa anthu amudera lawo.

Address

New Naperi
Blantyre

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Democratic Progressive Party - DPP posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share