18/08/2026
Tikudziwitsa alimi onse amene anagulitsa fodya wopitirira mulingo umene alimiwo anapatsidwa kuti ndalama za fodya ameneyu ziri ndi ife.
Alimi amene anagulitsa fodya ameneyu pasanadutse pa 14 August chaka chino alandira ndalama zawo pofika lachisanu pa 28 August.
Tikutsimikizira alimi onse okhudzidwa kuti alandira ndalama zawo mwachangu.
Ministry of Agriculture - Malawi TAMA Farmers Trust NASFAM