Ministry of Energy -Malawi

Ministry of Energy -Malawi Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Ministry of Energy -Malawi, Government Organization, chilembwe, Lilongwe.
(3)

The mission of the Ministry of Energy is “To fully satisfy public need for quality modern energy services by effectively governing and facilitating the development of a robust, sustainable and efficient private sector-driven energy industry.”

MLEMBI WAMKULU MU UNDUNA WA ZA MPHAMVU ANAYENDERA NDIKULIMBIKITSA OGWIRA NTCHITO KU PULOJEKITI YA ASCENTLero, Mlembi Wam...
01/06/2026

MLEMBI WAMKULU MU UNDUNA WA ZA MPHAMVU ANAYENDERA NDIKULIMBIKITSA OGWIRA NTCHITO KU PULOJEKITI YA ASCENT

Lero, Mlembi Wamkulu mu Unduna wa za Mphamvu, a Elvis Thodi, anayendera ofesi ya pulojekiti ya ASCENT pofuna kuwunika momwe ntchito zikuyendera, kulimbikitsa kufunika kogwira ntchito motsatira nthawi, komanso kumva mavuto omwe ogwira ntchito akukumana nawo. Ulendowu ukuwonetsa kudzipereka kwa Unduna pakuwonetsetsa kuti ASCENT ikupereka zotsatira zenizeni kwa a Malawi.

ASCENT (Accelerating Sustainable and Clean Energy Access Transformation) ndi pulojekiti yothandizidwa ndi Banki ya Dziko Lonse (World Bank) yomwe ikugwiridwa ntchito limodzi ndi Unduna wa za Mphamvu ndi ESCOM. Cholinga chake ndi kukulitsa mwayi wopeza magetsi komanso kulimbikitsa kugwiritsa ntchito mphamvu zophikira zotetezeka zosawononga chilengedwe kuti zitukule moyo wa anthu komanso chuma. A Thodi ,analimbikitsa mgwirizano wolimba pakati pa onse okhudzidwa kuti ntchito ziziyenda bwino.

Mu mau ake, Mlembiyu anatsindika kufunika kwa kuzipeleka kogwira ntchito mwaukadaulo, komanso kugwiritsa ntchito bwino chuma cha pulojekiti, kuti ASCENT ikwaniritse cholinga chake chokulitsa mwayi wopeza magetsi m’Malawi

Ngwee Ngwee Ngwee Fund

30/05/2026

Ndi udindo wathu kuteteza zipangizo za magesi.

PRESS RELEASE ON DIESEL SITUATION.
28/05/2026

PRESS RELEASE ON DIESEL SITUATION.

26/05/2026

Kumanga pafupi ndi mthambo za magesi ndikosaloledwa.

    #MAREP Phase 9 Brings Power to M’bande in ChikwawaThe Minister of Energy and Mining, Dr. Jean Mathanga, today graced...
26/05/2026


#

MAREP Phase 9 Brings Power to M’bande in Chikwawa

The Minister of Energy and Mining, Dr. Jean Mathanga, today graced the electricity switch-on ceremony for the M’bande MAREP site in Chikwawa, under the Malawi Rural Electrification Programme (MAREP) Phase 9.

Speaking during the event, Dr. Mathanga said it is the Government of Malawi’s commitment to ensure that people in rural areas have access to electricity.

“We are in Phase 9 where over 500 sites across the country will be reached, with Chikwawa alone benefiting from 22 sites.

"This government recognises the importance of such projects as they transform people’s lives,” said Mathanga.

Member of Parliament for Chikwawa Central Constituency, Jerald Bede, commended government for fulfilling its promise of bringing electricity to the area. He assured government that the people of Chikwawa Central will safeguard the infrastructure and ensure it is not vandalised.

Senior Traditional Authority Ndakwera also urged people in the area to remain vigilant and work together in protecting the development from theft and vandalism. He further called on chiefs to take an active role in safeguarding the project infrastructure.

Speaking earlier, the Principal Secretary for the Ministry of Energy and Mining, Elvis Thodi, said the M’bande Electrification Project in Chikwawa has cost K582 million more due to vandalism, which has occurred more than once.

MAREP is a Government Program in the Ministry of Energy and Mining with the aim of increasing access to electricity in rural and peri -urban areas.

The programme is implemented in phases and is currently in Phase 9.

Pictorial Highlights from the Minister of Energy and Mining, Dr. Jean Mathanga’s engagement during the Malawi Rural Elec...
26/05/2026

Pictorial Highlights from the Minister of Energy and Mining, Dr. Jean Mathanga’s engagement during the Malawi Rural Electrification Programme (MAREP) Phase 9 switch on event in Chikwawa District.

The programme continues to advance government’s efforts in expanding electricity access to rural communities across Malawi.

Department of Mining Mw

LIGHTING UP RURAL MALAWI: HON.DR JEAN MATHANGA SWITCHES ON MANDRADE TRADING CENTER.The Minister of Energy and Mining, Ho...
26/05/2026

LIGHTING UP RURAL MALAWI: HON.DR JEAN MATHANGA SWITCHES ON MANDRADE TRADING CENTER.

The Minister of Energy and Mining, Hon. Dr Jean Mathanga, M.P, today switched on electricity at Mandrade Trading Center in Chikwawa District. This marks a great step in Governmnet’s efforts to increase electricity access to rural communities across Malawi

Mandrade Trading center has been electrified under Malawi Rural Electrification Program (MAREP), phase 9 which will electrify more than 500 rural areas across the country except Likoma District, which is fully electrified. Under MAREP Phase 9, the Ministry has already electrified 22 areas in Chikwawa District alone.

Speaking during the switch on ceremony, Dr Mathanga urged community members and traditional leaders to ensure that the installed powerline is not vandalised. During construction phase, Mandrade site was vandalized more than once making the Ministry to use extra 582 Million Kwacha to reconstruct the powerline.

“Preparations for MAREP Phase 10 are already underway, with implementation expected to begin next year as Government pushes to connect even more Malawians to electricity” Dr. Mathanga stated.

While acknowledging low electricity generation capacity, Dr Mathanga highlighted that, beyond grid expansion, Government is also investing in large-scale power generation projects to improve electricity reliability across the country, including: development of a solar power plant in Salima by Electricity Generation Company (EGENCO) is developing a solar power plant in Salima, the Ministry is developing Mpatamanga Hydro project and Malawi is already importing from Zambia and will soon connect to Mozambique.


%ElectrificationBy2030 #

Department of Mining Mw

BEHIND THE SCENESThe Department of Energy Affairs conducting a community sensitisation meeting with community members fr...
25/05/2026

BEHIND THE SCENES

The Department of Energy Affairs conducting a community sensitisation meeting with community members from Ndakwera village in Chikwawa district on Malawi Rural Electrification Program (MAREP).

Community engagement is key in promoting ownership,enhanced public awareness and ensuring successful implementation on rural electrification projects.

#
%ElectrificityAcessBy2030 #

THIRANSIFOMA NDI CHUMA CHATHU – CHONDE ITETEZENI! Thilansifoma si chinthu chongoyima pachokha. Koma ndi mtima wa ntchito...
23/05/2026

THIRANSIFOMA NDI CHUMA CHATHU – CHONDE ITETEZENI!

Thilansifoma si chinthu chongoyima pachokha. Koma ndi mtima wa ntchito yofikisa magetsi mu nyumba komanso ma bizinesi amudera lanu Ikawonongeka kapena zipangizo zake zikabedwa, mabanja, mabizinesi, sukulu ndi zipatala zimakhudzidwa. kotero;

Musaigwire chifukwa chofuna kubapo zipangizo.

Tetezazani thilansifoma yanu ngati chuma chanu posatira izi;

Onesesani kuti anthu ogwira ntchito pa thilasifoma yomwe muli nayo pafupi ali ziphaso zowayenereza

Aziwiseni a polisi mukaona anthu okaikisa pa thiransifoma

Tiyeni tonse tigwirane manja poteteza zipangizo za magetsi kuti chitukuko chifike kwa aliyense.

yanu ndi chuma chanu

ESCOM

23/05/2026

Address

Chilembwe
Lilongwe

Opening Hours

Monday 08:00 - 16:30
Tuesday 08:00 - 16:30
Wednesday 08:00 - 16:30
Thursday 08:00 - 16:30
Friday 08:00 - 16:30

Telephone

+2651789488

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Ministry of Energy -Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Organization

Send a message to Ministry of Energy -Malawi:

Share